Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalira, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowa; yense anaola monga mwa njala yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Tsono atayesa ndi muyeso wa malita aŵiri, adaona kuti amene adaatola tambiri, sitidaŵatsalireko, amene adaatola pang'ono, sitidaŵathere. Aliyense adangotola tokwanira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo iwo atayeza ndi muyeso wa malita awiri, iye amene anatola zambiri sizinamutsalireko ndipo amene anatola pangʼono sizinamuchepere. Aliyense anatola zomukwanira kudya.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.


Ndipo kunena za mizindayo muiperekeyo yaoyao ya ana a Israele, okhala nayo yambiri mutengeko yambiri; okhala nayo pang'ono mutengeko pang'ono; onse operekako mizinda yao kwa Alevi monga mwa cholowa chao adachilandira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa