Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Aisraele adachitadi zimenezo. Ena adatola tambiri, koma ena pang'ono.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Aisraeli anachita zonse anawawuza. Ena anatola zambiri ena zochepa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:17
2 Mawu Ofanana  

Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.


Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa