Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:16 - Buku Lopatulika

16 Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Amenewo ndiwo mau walamulira Yehova, Aoleko yense monga mwa njala yake; munthu mmodzi omeri limodzi, monga momwe muli, yense atengere iwo m'hema mwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Chauta walamula kuti aliyense mwa inu atole womukwanira kudya, ndiye kuti malita aŵiri pa munthu mmodzi, malinga ndi chiŵerengero cha anthu onse a m'hema mwake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Yehova walamula kuti, ‘Aliyense atole zomukwanira kudya, malita awiri pa munthu mmodzi molingana ndi chiwerengero cha anthu amene ali mu tenti yanu.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anatero, naola wina wambiri, wina pang'ono.


Ndipo pamene anayesa ndi omeri, iye amene adaola wambiri sunamtsalire, ndi iye amene adaola pang'ono sunamsowe; yense anaola monga mwa njala yake.


Koma omeri ndilo limodzi la magawo khumi la efa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa