Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 10:18 - Buku Lopatulika

Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose adachoka kwa Farao kuja, nakapemphera kwa Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose anachoka kwa Farao nakapemphera kwa Yehova.

Onani mutuwo



Eksodo 10:18
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anabweza mphepo yolimbatu ya kumadzulo, imene inapita nalo dzombe niliponya mu Nyanja Yofiira: silinatsale dzombe limodzi pakati pa malire onse a Ejipito.


Ndipo Mose ndi Aroni anatuluka kwa Farao; ndi Mose anafuulira kwa Yehova kunena za achule amene adawaika pa Farao.


Pamenepo Farao anaitana Mose ndi Aroni, nati, Mundipembere Yehova, kuti andichotsere ine ndi anthu anga achulewo; ndipo ndidzalola anthu amuke, kuti amphere Yehova nsembe.


Koma Mose anati kwa Farao, Ulemu ndi wanu, wa ine ai; ndipembere inu ndi anyamata anu ndi anthu anu liti, kuti aonongeke achulewo, achokere inu ndi nyumba zanu, atsale m'mtsinje mokha?


Pamenepo anthu anafuulira kwa Mose; ndi Mose anapemphera kwa Yehova, ndi motowo unazima.


koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu;


dalitsani iwo akutemberera inu, pemphererani iwo akuchitira inu chipongwe.