Eksodo 8:8 - Buku Lopatulika8 Pamenepo Farao anaitana Mose ndi Aroni, nati, Mundipembere Yehova, kuti andichotsere ine ndi anthu anga achulewo; ndipo ndidzalola anthu amuke, kuti amphere Yehova nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamenepo Farao anaitana Mose ndi Aroni, nati, Mundipembere Yehova, kuti andichotsere ine ndi anthu anga achulewo; ndipo ndidzalola anthu amuke, kuti amphere Yehova nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pomwepo Farao adaitana Mose ndi Aroni naŵauza kuti, “Pempherani kwa Chauta kuti achuleŵa andichoke ine ndi anthu angaŵa, ndipo ndidzaŵalola anthu anu kuti apite kukapereka nsembe kwa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kenaka, Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni ndipo anati, “Pemphera kwa Yehova kuti achulewa achoke kwa ine ndi anthu anga, ndipo ine ndidzalola kuti anthu anu apite kukapereka nsembe kwa Yehova.” Onani mutuwo |