Mateyu 5:44 - Buku Lopatulika44 koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Chabwino, koma Ine ndikukuuzani kuti muzikonda adani anu ndipo muziŵapempherera amene amakuzunzani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Koma Ine ndikuwuzani kuti, ‘Kondani adani anu ndi kuwapempherera okuzunzani Onani mutuwo |