Mateyu 5:43 - Buku Lopatulika43 Munamva kuti kunanenedwa, Uzikondana ndi mnansi wako, ndi kumuda mdani wako: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Munamva kuti kunanenedwa, Uzikondana ndi mnansi wako, ndi kumuda mdani wako: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 “Mudamva kuti anthu akale aja adaaŵalamula kuti, ‘Ukonde mnzako, ndi kudana ndi mdani wako.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 “Munamva kuti, ‘Konda mnansi wako ndi kudana ndi mdani wako.’ Onani mutuwo |