Mateyu 5:42 - Buku Lopatulika42 Kwa iye wopempha iwe umpatse, ndipo kwa iye wofuna kukukongola usampotolokere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Kwa iye wopempha iwe umpatse, ndipo kwa iye wofuna kukukongola usampotolokere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Munthu akakupempha kanthu, uzimpatsa. Ndipo munthu akafuna kubwereka kanthu kwa iwe, usamkanize.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Wina akakupempha kanthu umupatse, ndipo wofuna kubwereka usamukanize. Onani mutuwo |