Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 10:18 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mose anachoka kwa Farao nakapemphera kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

18 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anatuluka kwa Farao, napemba Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mose adachoka kwa Farao kuja, nakapemphera kwa Chauta.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 10:18
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anasintha mphepo ija kuti ikhale ya mphamvu yochokera ku madzulo, ndipo inanyamula dzombe lija nʼkulikankhira mʼNyanja Yofiira. Panalibe dzombe ndi limodzi lomwe limene linatsala mu Igupto.


Mose ndi Aaroni anachoka, ndipo Mose anapemphera kwa Yehova kuti achotse achule amene anatumiza kwa Farao.


Kenaka, Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni ndipo anati, “Pemphera kwa Yehova kuti achulewa achoke kwa ine ndi anthu anga, ndipo ine ndidzalola kuti anthu anu apite kukapereka nsembe kwa Yehova.”


Mose anati kwa Farao, “Inu mungonditchulira nthawi imene mukufuna kuti ndikupempherereni, nduna zanu pamodzi ndi anthu anu kuti achule achoke mʼnyumba zanu ndi kuti atsale okhawo ali mu mtsinje wa Nailo.”


Anthuwo analira kwa Mose ndipo Moseyo atapemphera kwa Yehova, motowo unazima.


Koma Ine ndikuwuzani kuti, ‘Kondani adani anu ndi kuwapempherera okuzunzani


Dalitsani amene amakutembererani, apempherereni amene amakusautsani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa