Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 6:3 - Buku Lopatulika

Ndipo ichi tidzachita, akatilola Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ichi tidzachita, akatilola Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu akalola, tidzaterodi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Mulungu akalola, tidzaterodi.

Onani mutuwo



Ahebri 6:3
6 Mawu Ofanana  

koma anawatsanzika, nati, Akafuna Mulungu, ndidzabwera kwa inu; ndipo anachoka ku Efeso m'ngalawa.


kuti ndi chimwemwe ndikadze kwa inu mwa chifuniro cha Mulungu, ndi kupumula pamodzi ndi inu.


Pakuti sindifuna kukuonani tsopano popitirira; pakuti ndiyembekeza kukhala ndi inu nthawi, ngati alola Ambuye.


Koma ndidzafika kwa inu msanga, akandilola Ambuye; ndipo ndidzazindikira si mau a iwo odzitukumula, koma mphamvuyi.


Pakuti sikutheka kuwakonzanso, atembenuke mtima, iwo amene anaunikidwa pa nthawi yake, nalawa mphatso ya Kumwamba, nakhala olandirana naye Mzimu Woyera,


Mukadanena inu, Akalola Ambuye, ndipo tikakhala ndi moyo, tidzachita kakutikakuti.