Machitidwe a Atumwi 18:21 - Buku Lopatulika21 koma anawatsanzika, nati, Akafuna Mulungu, ndidzabwera kwa inu; ndipo anachoka ku Efeso m'ngalawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 koma anawatsanzika, nati, Akafuna Mulungu, ndidzabwera kwa inu; ndipo anachoka ku Efeso m'ngalawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Adaŵatsazika naŵauza kuti, “Mulungu akalola ndidzabweranso.” Atatero adachoka ku Efeso m'chombo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Koma pamene amachoka anawalonjeza kuti, “Ndidzabweranso Mulungu akalola.” Ndipo anakwera sitima ya pamadzi kuchoka ku Efeso. Onani mutuwo |