Ahebri 6:2 - Buku Lopatulika2 a chiphunzitso cha ubatizo, a kuika manja, a kuuka kwa akufa, ndi a chiweruziro chosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 a chiphunzitso cha ubatizo, a kuika manja, a kuuka kwa akufa, ndi a chiweruziro chosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa, ndi za chiweruzo chotsiriza. Koma tiyeni tipitirire mpaka tikafike pa kukhwima kwenikweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. Onani mutuwo |