Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 6:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo ichi tidzachita, akatilola Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo ichi tidzachita, akatilola Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mulungu akalola, tidzaterodi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ndipo Mulungu akalola, tidzaterodi.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 6:3
6 Mawu Ofanana  

koma anawatsanzika, nati, Akafuna Mulungu, ndidzabwera kwa inu; ndipo anachoka ku Efeso m'ngalawa.


kuti ndi chimwemwe ndikadze kwa inu mwa chifuniro cha Mulungu, ndi kupumula pamodzi ndi inu.


Pakuti sindifuna kukuonani tsopano popitirira; pakuti ndiyembekeza kukhala ndi inu nthawi, ngati alola Ambuye.


Koma ndidzafika kwa inu msanga, akandilola Ambuye; ndipo ndidzazindikira si mau a iwo odzitukumula, koma mphamvuyi.


Pakuti sikutheka kuwakonzanso, atembenuke mtima, iwo amene anaunikidwa pa nthawi yake, nalawa mphatso ya Kumwamba, nakhala olandirana naye Mzimu Woyera,


Mukadanena inu, Akalola Ambuye, ndipo tikakhala ndi moyo, tidzachita kakutikakuti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa