Yakobo 4:15 - Buku Lopatulika15 Mukadanena inu, Akalola Ambuye, ndipo tikakhala ndi moyo, tidzachita kakutikakuti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Mukadanena inu, Akalola Mulungu, ndipo tikakhala ndi moyo, tidzachita kakutikakuti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kwenikweni muyenera kumanena kuti, “Ambuye akalola, tikakhala ndi moyo, tidzachita chakutichakuti.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma inuyo muyenera kunena kuti, “Ambuye akalola, tikadzakhala ndi moyo, tidzachita zakutizakuti.” Onani mutuwo |