Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 4:16 - Buku Lopatulika

pakuti mu Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pakuti m'Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene ndinali ku Tesalonika, mudatumiza kangapo zondithandiza pa zosoŵa zanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti ngakhale pamene ndinali ku Tesalonika, munanditumizira kangapo zondithandiza pa zosowa zanga.

Onani mutuwo



Afilipi 4:16
4 Mawu Ofanana  

Pamene anapitirira pa Amfipoli, ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge wa Ayuda.


chifukwa tinafuna kudza kwa inu, inedi Paulo ndatero kamodzi kapena kawiri; koma Satana anatiletsa.


Pakuti mukumbukira, abale, chigwiritso chathu ndi chivuto chathu; pochita usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu, tinalalikira kwa inu Uthenga Wabwino wa Mulungu.


Ndipo anthu athu aphunzirenso asunge ntchito zabwino zofunika, kuti asakhale osabala zipatso.