Tito 3:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo anthu athu aphunzirenso asunge ntchito zabwino zofunika, kuti asakhale osabala zipatso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo anthu athu aphunzirenso asunge ntchito zabwino zofunika, kuti asakhale osabala zipatso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Anthu athunso aziphunzira kudzipereka pa ntchito zabwino, kuti azithandiza pamene pali kusoŵa kwenikweni. Azitero kuti moyo wao usakhale wopanda phindu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Anthu athu aphunzire kudzipereka pogwira ntchito zabwino, nʼcholinga chakuti athandize zinthu zimene zikufunika msangamsanga. Ndipo asakhale moyo osapindulitsa. Onani mutuwo |