Afilipi 4:17 - Buku Lopatulika17 Sikunena kuti nditsata choperekacho, komatu nditsata chipatso chakuchulukira ku chiwerengero chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Sikunena kuti nditsata choperekacho, komatu nditsata chipatso chakuchulukira ku chiwerengero chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Sikuti ndikuika mtima pa mphatso zanu ai, koma chimene ndikukhumba nchakuti pa zimene muli nazo, pawonjezedwe phindu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Osati ndikufuna mphatso zanu, koma ndikufuna kuti pa zimene muli nazo pawonjezerekepo phindu. Onani mutuwo |