Afilipi 4:16 - Buku Lopatulika16 pakuti mu Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 pakuti m'Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pamene ndinali ku Tesalonika, mudatumiza kangapo zondithandiza pa zosoŵa zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pakuti ngakhale pamene ndinali ku Tesalonika, munanditumizira kangapo zondithandiza pa zosowa zanga. Onani mutuwo |