Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Afilipi 4:16 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Pakuti ngakhale pamene ndinali ku Tesalonika, munanditumizira kangapo zondithandiza pa zosowa zanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

16 pakuti mu Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 pakuti m'Tesalonikanso munanditumizira pa chosowa changa kamodzi kapena kawiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Pamene ndinali ku Tesalonika, mudatumiza kangapo zondithandiza pa zosoŵa zanga.

Onani mutuwo Koperani




Afilipi 4:16
4 Mawu Ofanana  

Atadutsa ku Amfipoli ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge ya Ayuda.


Pakuti ife tinafuna kubweranso kwa inu, makamaka ine Paulo, ndinayesa kangapo koma Satana anatiletsa.


Abale, pakuti mukumbukira kugwira ntchito kwathu kwambiri ndi kuvutika; ife tinagwira ntchito usana ndi usiku ndi cholinga chakuti tisakhale cholemetsa, kwa aliyense pamene ife tinkalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu kwa inu.


Anthu athu aphunzire kudzipereka pogwira ntchito zabwino, nʼcholinga chakuti athandize zinthu zimene zikufunika msangamsanga. Ndipo asakhale moyo osapindulitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa