Machitidwe a Atumwi 17:1 - Buku Lopatulika1 Pamene anapitirira pa Amfipoli, ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge wa Ayuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamene anapitirira pa Amfipoli, ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge wa Ayuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Paulo ndi anzake aja adapitirira mizinda ya Amfipoli ndi Apoloniya nakafika ku Tesalonika. Kumeneko kunali nyumba yamapemphero ya Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atadutsa ku Amfipoli ndi Apoloniya, anafika ku Tesalonika, kumene kunali sunagoge ya Ayuda. Onani mutuwo |