Machitidwe a Atumwi 16:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo anatuluka m'ndendemo, nalowa m'nyumba ya Lidia: ndipo pamene anaona abale, anawasangalatsa, namuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo anatuluka m'ndendemo, nalowa m'nyumba ya Lidia: ndipo pamene anaona abale, anawasangalatsa, namuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Paulo ndi Silasi atatuluka m'ndende muja adapita kunyumba kwa Lidia. Kumeneko adaonana ndi abale, ndipo ataŵalimbikitsa, adachoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Paulo ndi Sila atatuluka mʼndende, anapita ku nyumba ya Lidiya, kumene anakumana ndi abale nawalimbikitsa. Kenaka anachoka. Onani mutuwo |