Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 4:3 - Buku Lopatulika

ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abeeroti adathaŵira ku Gitaimu, ndipo akhala akukhala nao kumeneko mpaka pano).

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

chifukwa anthu a ku Beeroti anathawira ku Gitaimu ndipo akhala ali kumeneko ngati alendo mpaka lero lino.

Onani mutuwo



2 Samueli 4:3
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Yonatani mwana wa Saulo, anali ndi mwana wamwamuna wopunduka mapazi. Iyeyu anali wa zaka zisanu muja inamveka mbiri ya Saulo ndi Yonatani yochokera ku Yezireele; ndipo mlezi wake adamnyamula nathawa; ndipo kunali pofulumira kuthawa, iye anagwa nakhala wopunduka. Dzina lake ndiye Mefiboseti.


Hazori, Rama, Gitaimu,


Ndipo pamene Aisraele akukhala tsidya lina la chigwa, ndi iwo akukhala tsidya la Yordani, anaona kuti Aisraele alikuthawa, ndi kuti Saulo ndi ana ake anafa, iwowa anasiya mizinda yao, nathawa; ndipo Afilisti anadza nakhala m'menemo.