Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 4:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 chifukwa anthu a ku Beeroti anathawira ku Gitaimu ndipo akhala ali kumeneko ngati alendo mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Abeeroti adathaŵira ku Gitaimu, ndipo akhala akukhala nao kumeneko mpaka pano).

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 4:3
3 Mawu Ofanana  

(Yonatani mwana wa Sauli anali ndi mwana wamwamuna amene anali wolumala mapazi ake onse awiri. Iye anali ndi zaka zisanu pamene nkhani ya Sauli ndi Yonatani inamveka kuchokera ku Yezireeli. Amene amamulera anamunyamula ndi kuthawa naye, koma pamene amachita zinthu mofulumira mwanayo anagwa ndipo analumala. Dzina lake linali Mefiboseti).


ku Hazori, Rama ndi Gitaimu,


Pamene Aisraeli amene anali tsidya lina la chigwa ndi amene anali tsidya la chigwa cha Yorodani anaona kuti gulu la ankhondo la Aisraeli lathawa komanso kuti Sauli ndi ana ake aphedwa, nawonso anathawa kusiya mizinda yawo. Ndipo Afilisti anabwera kudzakhalamo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa