2 Samueli 4:3 - Buku Lopatulika3 ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi Abeeroti anathawira ku Gitaimu; kumeneko amakhalira kufikira lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Abeeroti adathaŵira ku Gitaimu, ndipo akhala akukhala nao kumeneko mpaka pano). Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 chifukwa anthu a ku Beeroti anathawira ku Gitaimu ndipo akhala ali kumeneko ngati alendo mpaka lero lino. Onani mutuwo |