Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:2 - Buku Lopatulika

Mzimu wa Yehova unalankhula mwa ine, ndi mau ake anali pa lilime langa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mzimu wa Yehova unalankhula mwa ine, ndi mau ake anali pa lilime langa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Mzimu wa Chauta ukulankhula mwa ine, mau ake ali pakamwa panga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Mzimu wa Yehova unayankhula kudzera mwa ine; mawu ake anali pakamwa panga.

Onani mutuwo



2 Samueli 23:2
6 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano, mbuye wanga mfumu, maso a Aisraele onse ali pa inu, kuti muwauze amene adzakhala pa mpando wachifumu wa mbuye wanga mfumu atamuka iye.


Iye anati kwa iwo, Ndipo Davide mu Mzimu amtchula Iye bwanji Ambuye, nanena,


Davide mwini yekha anati mwa Mzimu Woyera, Ambuye anati kwa Ambuye wanga, Khala kudzanja langa lamanja, kufikira ndiwaika adani ako popondapo mapazi ako.


pakuti kale lonse chinenero sichinadze ndi chifuniro cha munthu; koma anthu a Mulungu, ogwidwa ndi Mzimu Woyera, analankhula.