Marko 12:36 - Buku Lopatulika36 Davide mwini yekha anati mwa Mzimu Woyera, Ambuye anati kwa Ambuye wanga, Khala kudzanja langa lamanja, kufikira ndiwaika adani ako popondapo mapazi ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Davide mwini yekha anati mwa Mzimu Woyera, Ambuye anati kwa Ambuye wanga, Khala kudzanja langa lamanja, kufikira ndiwaika adani ako popondapo mapazi ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Paja Davide, ndi nzeru zochokera kwa Mzimu Woyera, adati, “ ‘Chauta adauza Mbuye wanga kuti, Khala ku dzanja langa lamanja, mpaka nditasandutsa adani ako kuti akhale ngati chopondapo mapazi ako.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Pajatu Davide mwini wake, poyankhula mwa Mzimu Woyera, ananena kuti, “Ambuye anati kwa Ambuye anga: ‘Khalani pa dzanja langa lamanja kufikira nditayika adani anu pansi pa mapazi anu.’ Onani mutuwo |