2 Samueli 23:3 - Buku Lopatulika3 Mulungu wa Israele anati, Thanthwe la Israele linalankhula ndi ine; kudzakhala woweruza anthu molungama; woweruza m'kuopa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mulungu wa Israele anati, Thanthwe la Israele linalankhula ndi ine; kudzakhala woweruza anthu molungama; woweruza m'kuopa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mulungu wa Israele walankhula, Thanthwe la Israele landiwuza kuti, ‘Munthu amene amalamulira anthu mwachilungamo, kuŵalamulira molemekeza Mulungu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu wa Israeli anayankhula, Thanthwe la Israeli linati kwa ine: ‘Pamene munthu alamulira anthu mwachilungamo, pamene alamulira moopa Mulungu, Onani mutuwo |