Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:38 - Buku Lopatulika

Ndinapirikitsa adani anga, ndi kuwaononga; ndiponso sindinabwerere mpaka nditawatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinapirikitsa adani anga, ndi kuwaononga; ndiponso sindinabwerera mpaka nditawatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidalondola adani anga ndi kuŵapeza, sindidabwerere mpaka nditaŵagonjetsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ine ndinathamangitsa adani anga ndi kuwakantha; sindinabwerere mpaka iwo atawonongedwa.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:38
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene ana a Amoni anaona kuti Aaramu anathawa, iwonso anathawa pamaso pa Abisai, nalowa m'mzindamo. Ndipo Yowabu anabwera kuchokera kwa ana a Amoni, nafika ku Yerusalemu.


Ndinawatha ndi kuwapyoza, kuti sangathe kuuka, inde anagwa pansi pa mapazi anga.


Ndipo ndinali nawe kulikonse unamukako, ndi kuononga adani ako onse pamaso pako; ndipo ndidzamveketsa dzina lako, monga dzina la akulu ali padziko lapansi.


Mdani anati, Ndiwalondola, ndiwapeza, ndidzagawa zofunkha; ndidzakhuta nao mtima; ndidzasolola lupanga langa, dzanja langa lidzawaononga.


Koma m'zonsezi, ife tilakatu, mwa Iye amene anatikonda.