2 Samueli 22:39 - Buku Lopatulika39 Ndinawatha ndi kuwapyoza, kuti sangathe kuuka, inde anagwa pansi pa mapazi anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndinawatha ndi kuwapyoza, kuti sakhoza kuuka, inde anagwa pansi pa mapazi anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Ndidaŵakantha, ndidaŵagwetsa pansi, kotero kuti sadadzukenso, ndidaŵapondereza ndi mapazi anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Ndinawakantha kotheratu, ndipo sanathe kudzukanso; Iwo anagwera pansi pa mapazi anga. Onani mutuwo |