Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 11:14 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mawa Davide analembera Yowabu kalata, wopita naye Uriya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mawa Davide analembera Yowabu kalata, wopita naye Uriya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa mwake Davide adalembera Yowabu kalata, napatsira Uriya yemweyo kalatayo kuti akapereke.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmawa Davide analemba kalata kwa Yowabu ndipo anayitumiza ndi Uriya.

Onani mutuwo



2 Samueli 11:14
8 Mawu Ofanana  

Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni.


Ndiponso muletse kapolo wanu pa zodzitama; zisachite ufumu pa ine. Pamenepo ndidzakhala wangwiro, ndi wosachimwa cholakwa chachikulu.


Lilime lako likupanga zoipa; likunga lumo lakuthwa, lakuchita monyenga.


Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu aakulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya.


Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa?