Masalimo 62:9 - Buku Lopatulika9 Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu aakulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu akulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Anthu otsika ndi mpweya chabe, ngakhale anthu okwera ndi nthunzi chabe, onsewo ndi oluluka pa sikelo, ndi opepuka kupambana mpweya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anthu wamba ndi mpweya chabe; anthu apamwamba ndi bodza chabe; ngati atayezedwa pa sikelo iwo ndi chabe; iwowo pamodzi ndi mpweya ndi chabe Onani mutuwo |