Yeremiya 17:9 - Buku Lopatulika9 Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mtima wa munthu ndi chinthu chonyenga kwambiri kupambana zinthu zonse. Kuipa kwake nkosachizika. Kodi ndani angathe kuumvetsa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mtima wa munthu ndi wonyenga kupambana zinthu zonse ndipo kuyipa kwake nʼkosachizika. Ndani angathe kuwumvetsa? Onani mutuwo |