Yeremiya 17:10 - Buku Lopatulika10 Ine Yehova ndisanthula mtima, ndiyesa impso, kuti ndimpatse munthu yense monga mwa njira zake, monga zipatso za ntchito zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ine Yehova ndisanthula mtima, ndiyesa impso, kuti ndimpatse munthu yense monga mwa njira zake, monga zipatso za ntchito zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Koma Ine Chauta ndimafufuza maganizo ndi kuuyesa mtimawo. Ndimamchitira munthu aliyense molingana ndi makhalidwe ake ndiponso moyenerera ntchito zake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Ine Yehova ndimafufuza mtima ndi kuyesa maganizo, ndimachitira munthu aliyense molingana ndi makhalidwe ake ndiponso moyenera ntchito zake.” Onani mutuwo |