2 Samueli 12:9 - Buku Lopatulika9 Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa chiyani tsono wanyoza mau a Chauta, nuchita choipa pamaso pake? Wapha Uriya Muhiti ndi lupanga, ndipo wakwatira mkazi wake. Wamuphetsa Uriyayo kudzera mwa Aamoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nʼchifukwa chiyani unanyoza mawu a Yehova pochita chimene chili choyipa pamaso pake? Iwe unakantha Uriya Mhiti ndi lupanga ndipo unatenga mkazi wake kukhala wako. Uriyayo unamupha ndi lupanga la Aamoni. Onani mutuwo |