2 Samueli 12:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nʼchifukwa chiyani unanyoza mawu a Yehova pochita chimene chili choyipa pamaso pake? Iwe unakantha Uriya Mhiti ndi lupanga ndipo unatenga mkazi wake kukhala wako. Uriyayo unamupha ndi lupanga la Aamoni. Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa chiyani tsono wanyoza mau a Chauta, nuchita choipa pamaso pake? Wapha Uriya Muhiti ndi lupanga, ndipo wakwatira mkazi wake. Wamuphetsa Uriyayo kudzera mwa Aamoni. Onani mutuwo |