Masalimo 52:2 - Buku Lopatulika2 Lilime lako likupanga zoipa; likunga lumo lakuthwa, lakuchita monyenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Lilime lako likupanga zoipa; likunga lumo lakuthwa, lakuchita monyenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsiku lonse umakhalira kusinkhasinkha za kuwononga ena, lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nkunyenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena; lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nʼkunyenga. Onani mutuwo |