Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 1:25 - Buku Lopatulika

Ha! Amphamvuwo anagwa pakati pa nkhondo! Yonatani anaphedwa pamisanje pako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ha! Amphamvuwo anagwa pakati pa nkhondo! Yonatani anaphedwa pamisanje pako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ha! Kani amphamvu agwa motere! Yonatani ali gone, atafa pa zitunda zako zachipembedzo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Taonani amphamvu agwa ku nkhondo! Yonatani wagona ataphedwa ku zitunda.

Onani mutuwo



2 Samueli 1:25
6 Mawu Ofanana  

Ulemerero wako, Israele, unaphedwa pa misanje yako. Ha! Adagwa amphamvu!


Ana aakazi inu a Israele, mulirire Saulo, amene anakuvekani ndi zofiira zokometsetsa, amene anaika zokometsetsa zagolide pa zovala zanu.


Ha! Amphamvuwo anagwa, ndi zida za nkhondo zinaonongeka.


Korona wagwa pamutu pathu; kalanga ife! Pakuti tinachimwa.


Zebuloni ndiwo anthu anataya moyo wao mpaka imfa, Nafutali yemwe poponyana pamisanje.