Maliro 5:16 - Buku Lopatulika16 Korona wagwa pamutu pathu; kalanga ife! Pakuti tinachimwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Korona wagwa pamutu pathu; kalanga ife! Pakuti tinachimwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chisoti chathu chaufumu chachoka kumutu, kugwa pansi. Tsoka kwa ife, chifukwa tachimwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Chipewa chathu chaufumu chagwa pamutu pathu. Tsoka kwa ife, chifukwa tachimwa! Onani mutuwo |