2 Samueli 1:27 - Buku Lopatulika27 Ha! Amphamvuwo anagwa, ndi zida za nkhondo zinaonongeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ha! Amphamvuwo anagwa, ndi zida za nkhondo zinaonengeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 “Ha! Kani amphamvu agwa motere, zida zao zankhondo nkuwonongeka!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Taonani amphamvu agwa! Zida zankhondo zawonongeka!” Onani mutuwo |