Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 6:1 - Buku Lopatulika

Ndipo likasa la Yehova linakhala ku dziko la Afilisti miyezi isanu ndi iwiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo likasa la Yehova linakhala ku dziko la Afilisti miyezi isanu ndi iwiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Bokosi lachipangano la Chauta lidakhala m'dziko la Afilisti miyezi isanu ndi iŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Bokosi la Yehova linakhala mʼdziko la Afilisti kwa miyezi isanu ndi iwiri.

Onani mutuwo



1 Samueli 6:1
6 Mawu Ofanana  

napereka mphamvu yake mu ukapolo, ndi ulemerero wake m'dzanja la msautsi.


Ndipo Afilisti anatenga likasa la Mulungu, nachoka nalo ku Ebenezeri, napita ku Asidodi.


Ndipo amene anapanda kufa anagwidwa ndi mafundowo; ndi kulira kwa mzindawo kunakwera kumwamba.


Ndipo pakuuka a ku Asidodi mamawa taonani Dagoni adagwa pansi, nagona chafufumimba patsogolo pa likasa la Yehova. Ndipo iwo anatenga Dagoni namuimikanso m'malo mwake.


Ndipo Afilistiwo anaitana ansembe ndi oombeza, nati, Tichitenji ndi likasa la Yehova? Mutidziwitse chimene tilitumize nacho kumalo kwake.