1 Samueli 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo pakuuka a ku Asidodi mamawa taonani Dagoni adagwa pansi, nagona chafufumimba patsogolo pa likasa la Yehova. Ndipo iwo anatenga Dagoni namuimikanso m'malo mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo pakuuka a ku Asidodi mamawa taonani Dagoni adagwa pansi, nagona chafufumimba patsogolo pa likasa la Yehova. Ndipo iwo anatenga Dagoni namuimikanso m'malo mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 M'maŵa mwake anthu a ku Asidodi atadzuka m'mamaŵa, adangoona Dagoni atagwa chafufumimba patsogolo pa Bokosi lachipanganolo. Apo anthuwo adatenga fanolo, naliikanso pamalo pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu a ku Asidodi atadzuka mmawa mwake, anangoona Dagoni atagwa pansi chafufumimba pamaso pa Bokosi la Yehova! Iwo anatenga Dagoni ndi kumuyimika pamalo pake. Onani mutuwo |