Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 19:12 - Buku Lopatulika

Chomwecho Mikala anamtsitsira Davide pazenera, namuka iye, nathawa, napulumuka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chomwecho Mikala anamtsitsira Davide pazenera, namuka iye, nathawa, napulumuka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Mikala adamtulutsira Davideyo pa windo, ndipo adathaŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Mikala anamutulutsira Davide pa zenera, ndipo anathawa ndi kupulumuka.

Onani mutuwo



1 Samueli 19:12
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anyamata a Abisalomu anafika kunyumba kwa mkaziyo; nati, Ali kuti Ahimaazi ndi Yonatani? Ndipo mkaziyo ananena nao, Anaoloka kamtsinje kamadzi. Ndipo atawafunafuna, osawapeza, anabwerera kunka ku Yerusalemu.


Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.


Pamenepo anawatsitsa pazenera ndi chingwe; popeza nyumba yake inali pa linga la mzinda, nakhala iye palingapo.


Ndipo ana a Saulo ndiwo Yonatani, ndi Isivi, ndi Malikisuwa; ndi maina a ana aakazi ake awiri ndi awa: dzina la woyamba ndiye Merabi, ndi dzina la mng'ono wake ndiye Mikala;