Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 15:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Saulo anamemeza anthu, nawawerenga ku Telaimu, akuyenda pansi zikwi mazana awiri, ndi a kwa Yuda anthu zikwi khumi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Saulo anamemeza anthu, nawawerenga ku Telaimu, akuyenda pansi zikwi mazana awiri, ndi a kwa Yuda anthu zikwi khumi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Saulo adaitana ankhondo ake, naŵaŵerenga ku Telaimu. Ankhondo oyenda pansi analipo 200,000, ankhondo a ku Yuda analipo 10,000 pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kotero Sauli anayitana ankhondo ake nawawerenga ku Telaimu. Ankhondo oyenda pansi analipo 200,000 ndipo mwa iwowa 10,000 anali a fuko la Yuda.

Onani mutuwo



1 Samueli 15:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu Yehoramu anatuluka mu Samariya nthawi yomweyo, namemeza Aisraele onse.


Zifi ndi Telemu ndi Bealoti;


Ndipo anawawerenga ku Bezeki; ndipo ana a Israele anali zikwi mazana atatu, ndi anthu a Yuda ndiwo zikwi makumi atatu.


Ndipo Samuele anauka nachoka ku Giligala kunka ku Gibea wa ku Benjamini. Ndipo Saulo anawerenga anthu amene anali naye, monga mazana asanu ndi limodzi.


Ndipo Saulo anafika kumzinda wa Amaleke, nalalira kuchigwa.