1 Samueli 15:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Saulo anafika kumzinda wa Amaleke, nalalira kuchigwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Saulo anafika kumudzi wa Amaleke, nalalira kuchigwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndipo Saulo adafika ku mzinda wa Aamaleke, naubisalira m'khwaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Sauli anapita ku mzinda wa Aamaleki nawubisalira mʼkhwawa. Onani mutuwo |