Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 7:1 - Buku Lopatulika

Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsopano ndiyankhe zimene mudandifunsa m'kalata yanu. Nkwabwino kuti munthu asakwatire,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano pa zinthu zomwe munandilembera nʼkwabwino kuti munthu asakwatire.

Onani mutuwo



1 Akorinto 7:1
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anati kwa iye m'kulota, Inde ndidziwa Ine, kuti wachita icho ndi mtima wangwiro, ndipo Inenso ndinakuletsa iwe kuti usandichimwire ine: chifukwa chake sindinakuloleze iwe kuti umkhudze mkaziyo.


Chomwecho wolowa kwa mkazi wa mnzake; womkhudzayo sadzapulumuka chilango.


Koma chifukwa cha madama munthu yense akhale naye mkazi wa iye yekha, ndi mkazi yense akhale naye mwamuna wa iye yekha.


Koma ndinena kwa osakwatira, ndi kwa akazi amasiye, kuti kuli bwino kwa iwo ngati akhala monganso ine.


Maso ako akhale pamunda achekawo, ndi kuwatsata; kodi sindinawauze anyamata asakukhudze? Ndipo ukamva ludzu, muka kumitsuko, ukamweko otunga anyamatawo,