1 Akorinto 6:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti munagulidwa ndi mtengo wake wapatali; chifukwa chake lemekezani Mulungu m'thupi lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti munagulidwa ndi mtengo wake wapatali; chifukwa chake lemekezani Mulungu m'thupi lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mulungu adakugulani ndi mtengo wapatali, tsono muzimlemekeza ndi matupi anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ndinu ochita kugulidwa. Nʼchifukwa chake lemekezani Mulungu mʼthupi lanu. Onani mutuwo |