Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:1
4 Mawu Ofanana  

Choncho Aisraeli anachita monga Yehova analamulira Mose.


Tsono tenti ya msonkhano ndi msasa wa Alevi zidzakhala pakati pa misasayo. Iwo adzasamuka monga momwe anamangira misasa yawo, aliyense pa malo ake pamene pali mbendera yake.


“Aisraeli azimanga misasa yawo mozungulira tenti ya msonkhano motalikira pangʼono. Munthu aliyense amange pamene pali mbendera ya fuko lake.”


Kenaka atsogoleri a Aisraeli, akuluakulu a mabanja omwe ankayangʼanira mafuko a anthu omwe anawawerenga aja, anachita chopereka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa