Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:1
4 Mawu Ofanana  

Momwemo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose; anachita momwemo.


Pamenepo khamu la Alevi azimuka nacho chihema chokomanako, pakati pa makamu; monga amamanga mahema ao, momwemo azimuka ulendo wao, munthu yense pamalo pake, monga mwa mbendera zao.


Ana a Israele azimanga mahema ao yense ku mbendera yake, ya chizindikiro cha nyumba ya kholo lake; amange mahema ao popenyana ndi chihema chokomanako pozungulira.


akalonga a Israele, akulu a nyumba za makolo ao, anapereka nsembe, ndiwo akalonga a mafuko akuyang'anira owerengedwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa