Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 1:54 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Choncho Aisraeli anachita monga Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

54 Momwemo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose; anachita momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Momwemo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose; anachita momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Umu ndi m'mene adachitira Aisraele. Adachita zonse monga momwe Chauta adaalamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:54
17 Mawu Ofanana  

Aisraeli anachita monga momwe Yehova analamulira Mose ndi Aaroni.


Tsopano ntchito yonse ya tenti ya msonkhano inatha. Aisraeli anachita zonse monga momwe Yehova analamulira Mose.


Mose anayendera ntchitoyo ndipo anaona kuti anayichita monga momwe Yehova analamulira. Kotero Mose anawadalitsa.


Mose anachita zonse monga Yehova anamulamulira.


Iwo amasamba nthawi zonse akamalowa mu tenti ya msonkhano kapena kuyandikira guwa lansembe monga Yehova analamulira Mose.


monga momwe Yehova analamulira Mose. Motero iyeyo anawawerenga mʼchipululu cha Sinai:


Alevi nawonso, azimanga matenti awo mozungulira tenti yopatulika kuti chilango chisagwere Aisraeli onse. Ndipo Alevi aziyangʼanira ndi kusamalira tenti yopatulikayo.”


Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:


Choncho Aisraeli anachita zonse zomwe Yehova analamulira Mose. Umo ndi momwe amamangira misasa yawo pamene panali mbendera zawo, ndipo ankasamuka monga mwa mafuko a makolo awo.


Choncho ana aakazi a Zelofehadi anachita monga Yehova analamulira Mose.


Mose, Aaroni pamodzi ndi gulu lonse la Israeli anachita kwa Alevi monga momwe Yehova analamulira Mose.


Ngakhale mtambo ukhale pa chihema masiku awiri kapena mwezi kapena chaka, Aisraeli ankakhalabe pa msasa osachoka. Koma ukachoka, ankasamuka.


ndipo anachitadi Paskayo mʼchipululu cha Sinai madzulo a tsiku la 14 la mwezi woyamba. Aisraeli anachita zonse monga momwe Yehova analamulira Mose.


ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.”


Onetsetsani kuti mukuchita zimene ndikukulamulirani. Musawonjezerepo kapena kuchotserapo.


Koma Samueli anayankha kuti, “Kodi Yehova amakondwera ndi nsembe zopsereza ndi nsembe zina kapena kumvera mawu a ake? Taona, kumvera ndi kwabwino kuposa nsembe, ndipo kutchera khutu ndi kwabwino kuposa kupereka mafuta a nkhosa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa