Eksodo 2:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mlongo wake wa mwanayo anayima pataliko kuti aone chimene chidzamuchitikira mwanayo. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo mlongo wake anaima patali, adziwe chomwe adzamchitira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndipo mlongo wake wa mwanayo adaimirira pafupi namangopenyetsetsa, kuti aone zimene zimchitikire mwanayo. Onani mutuwo |